Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 32:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kumbukilani Abrahamu, Isake ndi Israyeli, atumiki anu, amene munawalumbirira ndi kudzichula nokha, amene munanena nao, Ndidzacurukitsa mbeu zanu ngati nyenyezi za kuthambo, ndi dziko ili lonse ndanenali ndidzapatsa mbeu zanu, likhale colowa cao nthawi zonse.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 32

Onani Eksodo 32:13 nkhani