Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 32:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Mose anapemba kwa Yehova Mulungu wace, nati, Yehova, mtima wanu upserenji pa anthu anu, amene munawaturutsa m'dziko la Aigupto ndi mphamvu yaikuru, ndi dzanja lolimba?

Werengani mutu wathunthu Eksodo 32

Onani Eksodo 32:11 nkhani