Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 31:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Za amisiri opanga nchitoyi, Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,

2. Taona ndaitana ndi kumchula dzina lace, Bezaleli, mwana wa Uri, mwana wa Huri, wa pfuke la Yuda;

3. ndipo ndamdzaza nd mzimu wa Mulungu, ndi luso, ndi nzeru, ndi cidziwitso, ndi m'nchito ziri zonse,

4. kulingirira nchito zaluso, kucita ndi golidi ndi siliva ndi mkuwa,

Werengani mutu wathunthu Eksodo 31