Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 29:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo utapeko pa mwazi wa ng'ombe yamphongo, ndi kuupaka pa nyanga za guwa la nsembe ndi cala cako, nutsanulire mwazi wonse pa tsinde la guwa la nsembe.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 29

Onani Eksodo 29:12 nkhani