Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 22:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Munthu akadyetsa coweta pabusa kapena pa munda wamphesa, atamasula coweta cace, ndipo citadya podyetsa pa mwini wace; alipe podyetsa pace poposa, ndi munda wa mphesa wace woposa.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 22

Onani Eksodo 22:5 nkhani