Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 22:30-31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

30. Uzitero nazo ng'ombe zako, ndi nkhosa zako; masiku asanu ndi atatu akhale ndi amai wace; tsiku lacisanu ndi citatu uzimpereka kwa Ine.

31. Ndipo muzindikhalira Ine anthu opatulika; cifukwa cace musamadya nyama yojiwa kuthengo; itayireni agaru.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 22