Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 2:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma pamene sanathe kumbisanso, anamtengera kabokosi kagumbwa, napakapo nkhunga ndi phula; naikamo mwanayo, nakaika pakati pa mabango m'mbali mwa nyanja.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 2

Onani Eksodo 2:3 nkhani