Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 2:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo atakula mwanayo, anapita naye kwa mwana wamkazi wa Farao, ndipo iye anakhala mwana wace. Ndipo anamucha dzina lace Mose, nati, Cifukwa ndinambvuula m'madzi.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 2

Onani Eksodo 2:10 nkhani