Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 17:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pomwepo anthu anamva ludzu lokhumba madzi; ndi anthu anadandaulira Mose, nati, Munatikwezeranji kucokera ku Aigupto, kudzatipha ife ndi ana athu ndi zoweta zathu ndi ludzu?

Werengani mutu wathunthu Eksodo 17

Onani Eksodo 17:3 nkhani