Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 16:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nanenanso Mose, Pakukupatsani Yehova nyama ya kudya madzulo, ndi mkate wokhuta m'mawa, atero popeza Yehova adamva madandaulo anu amene mumdandaulira nao. Koma ife ndife ciani? simulikudandaulira ife koma Yehova.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 16

Onani Eksodo 16:8 nkhani