Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 14:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anauza mfumu ya Aigupto kuti anthu adathawa; ndi mtima wa Farao ndi wa anyamata ace inasandulikira anthuwo, ndipo anati, Ici nciani tacita, kuti talola Israyeli amuke osatigwiriranso nchito?

Werengani mutu wathunthu Eksodo 14

Onani Eksodo 14:5 nkhani