Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 13:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo cizikhala ndi iwe ngati cizindikilo pa dzanja lako, ndi cikumbutso pakati pa maso ako; kuti cilamulo ca Yehova cikhale m'kamwa mwako; pakuti Yehova anakuturutsa m'Aigupto ndi dzanja lamphamvu.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 13

Onani Eksodo 13:9 nkhani