Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 13:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo kunakhala, pamene Farao anadziumitsa kuti tisamuke, Yehova anawapha onse oyamba kubadwa m'dziko la Aigupto, kuyambira oyamba a anthu, kufikira oyamba a zoweta; cifukwa cace ndimphera nsembe Yehova zazimuna zoyamba kubadwa zonse; koma oyamba onse a ana anga ndiwaombola.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 13

Onani Eksodo 13:15 nkhani