Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 12:42 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndiwo usiku wosungira Yehova ndithu, cifukwa ca kuwaturutsa m'dziko la Aigupto; usiku womwe uno ukhale wosungira Yehova ana onse a Israyeli ku mibadwo yao.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 12

Onani Eksodo 12:42 nkhani