Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 12:37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ana a Israyeli anayenda ulendo wakucokera ku Ramese kufikira ku Sukoti, zikwi mazana asanu ndi limodzi oyenda okha, ndiwo amuna, osawerenga ana.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 12

Onani Eksodo 12:37 nkhani