Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 10:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anabweza mphepo yolimbatu ya kumadzulo, imene inapita nalo dzombe niliponya m'Nyanja Yofiira: silinatsala dzombe limodzi pakati pa malire onse a Aigupto.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 10

Onani Eksodo 10:19 nkhani