Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 1:20-22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

20. Potero Mulungu anawacitira zabwino anamwino; ndipo anthuwo anacuruka, nakhala nazo mphamvu zazikuru.

21. Ndipo kunatero kuti, popeza anamwino anaopa Mulungu, iye anawamangitsira mabanja.

22. Ndipo Farao analamulira anthu ace onse, ndi kuti, Ana amuna onse akabadwa aponyeni m'nyanja, koma ana akazi onse alekeni amovo.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 1