Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Eksodo 1:1-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. NDIPO maina a ana a Israyeli, amene analowa m'Aigupto ndi Yakobo ndi awa, analowa munthu ndi banja lace:

2. Rubeni, Simeoni, Levi ndi Yuda;

3. Isakara, Zebuloni, ndi Benjamini;

4. Dani ndi Nafitali, Gadi ndi Aseri.

5. Ndipo amoyo onse amene anaturuka m'cuunomwace mwa Yakobo ndiwo makumi asanu ndi awiri; kama Yosefe anali m'Aigupto.

6. Ndipo anafa Yosefe, ndi abale ace onse, ndi mbadwo uwo wonse.

Werengani mutu wathunthu Eksodo 1