Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 6:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo muziwaphunzitsa mwacangu kwa ana anu, ndi kuwalankhula awa pokhala pansi m'nyumba zanu, ndi poyenda inu panjira, ndi pogona inu pansi, ndi pouka inu.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 6

Onani Deuteronomo 6:7 nkhani