Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 5:28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anamva mau a kunena kwanu, pamene munanena ndi ine; ndipo Yehova anati kwa ine, Ndidamva mau a kunena kwao kwa anthu awa, amene ananena ndi iwe; cokoma cokha cokha adanenaci.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 5

Onani Deuteronomo 5:28 nkhani