Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 34:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anati kwa iye, Si ili dziko ndinalumbirira Abrahamu, Isake, ndi Yakobo, ndi kuti, Ndidzalipereka kwa mbeu zako. Ndinakuonetsa ili m'maso, koma sudzaolokako.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 34

Onani Deuteronomo 34:4 nkhani