Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 33:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Woyamba kubadwa wa ng'ombe yace, ulemerero ndi wace;Nyanga zace ndizo nyanga zanjati;Adzatunga nazo mitundu ya anthu pamodzi, kufikira malekezero a dziko lapansi.Iwo ndiwo zikwi khumi za Efraimu,Iwo ndiwo zikwi za Manase.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 33

Onani Deuteronomo 33:17 nkhani