Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 31:28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndisonkhanitsire akuru onse a mapfuko anu, ndi akapitao anu, kuti ndinene mau awa m'makutu mwao, ndi kucititsa mboni kumwamba ndi dziko lapansi zitsutse iwo.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 31

Onani Deuteronomo 31:28 nkhani