Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 3:28-29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

28. Koma langiza Yoswa, dioloketu numlimbitse mtima, ndi kumkhwimitsa, pakuti adzaoloka pamaso pa anthu awa, nadzawalandiritsa dziko ulionali likhale lao lao.

29. Potero tinakhala m'cigwamo pandunji pa Beti Peori.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 3