Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 28:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova adzakukhazikirani yekha mtundu wa anthu wopatulika, monga anakulumbirirani; ngati mudzasunga malamulo a Yehova Mulungu wanu, ndi kuyenda m'njira zace.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 28

Onani Deuteronomo 28:9 nkhani