Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 28:29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo mudzafufuza usana, monga wakhungu amafufuza mumdima, ndipo simudzapindula nazo njira zanu; koma mudzakhala wopsinjika, nadzakuberani masiku onse, wopanda wina wakukupulumutsani.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 28

Onani Deuteronomo 28:29 nkhani