Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 28:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Yehova adzakukanthani ndi nthenda yoondetsa ya cifuwa, ndi malungo, ndi cibayo, ndi kutentha thupi, ndi lupanga, cinsikwi ndi cinoni; ndipo zidzakutsatani kufikira mwatayika.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 28

Onani Deuteronomo 28:22 nkhani