Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 28:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova adzakuyesani mutu, si mcira ai; ndipo mudzakhala wa pamwamba pokha, si wapansi ai; ngati mudzamvera malamulo a Yehova Mulungu wanu, amene ndikuuzani lero, kuwasunga ndi kuwacita;

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 28

Onani Deuteronomo 28:13 nkhani