Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 26:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Penyani muli mokhalamo mwanu mopatulika, m'mwamba, ndipo dalitseni anthu anu Israyeli, ndi nthaka imene munatipatsa, monga munalumbirira makolo athu, dziko moyenda mkaka ndi uci ngati madzi.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 26

Onani Deuteronomo 26:15 nkhani