Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 22:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo, taonani, wamneneza zoutsa mbiri yamanyazi, ndi kuti, Sindinapeza zizindikilo za unamwali wace in'mwana wako wamkazi; koma si izi zizindikilo za unamwali wa mwana wanga wamkazi. Ndipo azifunyulula cobvalaco pamaso pa akulu a mudziwo.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 22

Onani Deuteronomo 22:17 nkhani