Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 20:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo akapitao anene ndi anthu, ndi kuti, Ndani munthuyo anamanga nyumba yatsopano, osalowamo? amuke nabwerere kunyumba kwace, kuti angafe kunkhondo nangalowemo munthu wina.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 20

Onani Deuteronomo 20:5 nkhani