Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 2:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndiwo anthu akuru, ndi ambiri, ndi atalitali, monga Aanaki; koma Yehova anawaononga pamaso pao; ndipo analanda dziko lao, nakhala m'malo mwao;

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 2

Onani Deuteronomo 2:21 nkhani