Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 2:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo tinabwerera, ndi kuyenda kumka kucipululu, kutsata njira ya Nyanja Yofiira, monga Yehova adanena ndi ine; ndipo tinapaza phiri la Seiri masiku ambiri.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 2

Onani Deuteronomo 2:1 nkhani