Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 19:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Musamasendeza malire a mnansi wanu, amene adawaika iwo a kale lomwe, m'colowa canu mudzalandiraci, m'dziko limene Yehova Mulungu wanu akupatsani likhale lanu lanu.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 19

Onani Deuteronomo 19:14 nkhani