11. Kapena wotsirika, kapena wobwebweta, kapena wopenduza, kapena wofunsira akufa.
12. Popeza ali yense wakucita izi Yehova anyansidwa naye; ndipo cifukwa ca zonyansa izi Yehova Mulungu wanu awapitikitsa pamaso panu.
13. Mukhale angwiro ndi Yehova Mulungu wanu.