Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 17:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mutakalowa m'dziko limene Yehova Mulungu wanu akupatsani, ndi kulilandira lanu lanu, ndi kukhalamo; ndipo mukanena, Tidziikire mfumu, monga amitundu onse akutizinga;

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 17

Onani Deuteronomo 17:14 nkhani