Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 11:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo muziwaphunzitsa ana anu, ndi kuwalankhula awa pokhala inu pansi m'nyumba mwanu, ndi poyenda inu panjira, ndi pogona inu pansi, ndi pakuuka inu pomwe.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 11

Onani Deuteronomo 11:19 nkhani