Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 10:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo tsopano, Israyeli, Yehova Mulungu wanu afunanji nanu, koma kuti muziopa Yehova Mulungu wanu, kuyenda m'njira zace zonse, ndi kukonda, ndi kutumikira Yehova Mulungu wanundimtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse,

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 10

Onani Deuteronomo 10:12 nkhani