Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 1:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

AWA ndi mau amene Mose ananena kwa Israyeli wonse, tsidya la Yordano m'cipululu, m'cidikha ca pandunji pa Sufu, pakati pa Parani, ndi Tofeli, ndi Labani, ndi Hazeroti, ndi Di Zahabi.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 1

Onani Deuteronomo 1:1 nkhani