Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 9:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ambuye, cilungamo nca Inu, koma kwa ife manyazi a nkhope yathu, monga lero lino; kwa anthu a Yuda, ndi kwa okhala m'Yerusalemu, ndi kwa Aisrayeli onse okhala pafupi ndi okhala kutali, ku maiko onse kumene mudawaingira, cifukwa ca kulakwa kwao anakulakwirani nako.

Werengani mutu wathunthu Danieli 9

Onani Danieli 9:7 nkhani