Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 9:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinapemphera kwa Yehova Mulungu wanga ndi kubvomereza, ndi kuti, Ambuye Mulungu wamkuru ndi woopsa, wakuwasungira pangano ndi cifundo iwo akukukondani, ndi kusunga malamulo anu,

Werengani mutu wathunthu Danieli 9

Onani Danieli 9:4 nkhani