Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 9:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anakwaniritsa mau ace adanenawo, kutitsutsa ife ndi oweruza athu otiweruza, ndi kutitengera coipa cacikuru; pakuti pansi pa thambo lonse sipanacitika monga umo panacitikira Yerusalemu.

Werengani mutu wathunthu Danieli 9

Onani Danieli 9:12 nkhani