Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 5:30-31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

30. Usiku womwewo Belisazara mfumu ya Akasidi anaphedwa.

31. Ndipo Dariyo Mmedi analandira ufumuwo ali wa zaka makumi asanu ndi limodzi mphambu ziwiri.

Werengani mutu wathunthu Danieli 5