Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 5:27-31 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

27. TEKEL, Mwayesedwa pamiyeso, nimupezeka mwaperewera.

28. PERES, ufumu wanu wagawika, nuperekedwa kwa Amedi ndi Aperisi.

29. Pamenepo Belisazara analamulira, ndipo anabveka Danieli cibakuwa, ndi unyolo wagolidi m'khosi mwace, nalalikira za iye kuti ndiye wolamulira wacitatu m'ufumumo.

30. Usiku womwewo Belisazara mfumu ya Akasidi anaphedwa.

31. Ndipo Dariyo Mmedi analandira ufumuwo ali wa zaka makumi asanu ndi limodzi mphambu ziwiri.

Werengani mutu wathunthu Danieli 5