Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 5:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ndamva ine za iwe, kuti ukhoza kutanthauzira mau, ndi kumasula mfundo; tsono ukakhoza kuwerenga lembalo, ndi kundidziwitsa kumasulira kwace, udzabvekedwa cibakuwa, ndi unyolo wagolidi m'khosi mwako; nudzakhala wolamulira wacitatu m'ufumuwo.

Werengani mutu wathunthu Danieli 5

Onani Danieli 5:16 nkhani