Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 3:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo mfumu Nebukadinezara anadabwa, nauka msanga, nanena nati kwa mandoda ace, Kodi sitinaponya amuna atatu omangidwa m'kati mwa moto? Anayankha nati kwa mfumu, Inde mfumu.

Werengani mutu wathunthu Danieli 3

Onani Danieli 3:24 nkhani