Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Danieli 3:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo amuna awa anamangidwa ali cibvalire zopfunda zao, maraya ao, ndi nduwira zao, ndi zobvala zao zina; naponyedwa m'kati mwa ng'anjo yotentha yamoto.

Werengani mutu wathunthu Danieli 3

Onani Danieli 3:21 nkhani