Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Amosi 9:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti taonani, ndidzalamulira, ndipo ndidzapeta nyumba ya Israyeli mwa amitundu onse, monga apeta tirigu m'licero; koma silidzagwa pansi diso, ndi limodzi lonse.

Werengani mutu wathunthu Amosi 9

Onani Amosi 9:9 nkhani