Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Amosi 8:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kodi dziko silidzanjenjemera cifukwa ca ici, ndi kulira ali yense wokhalamo? inde lidzakwera lonseli ngati madzi a m'mtsinje; lidzagwedezeka, ndi kutsikanso ngati mtsinje wa Aigupto,

Werengani mutu wathunthu Amosi 8

Onani Amosi 8:8 nkhani