Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Amosi 6:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pitani ku Kaline, nimuone; kucokera komweko mupite ku Hamati wamkulu mutsikire ku Gati wa Afilisti; kodi awo ndi okoma koposa maufumu ano? kapena malire ao aposa malire anu?

Werengani mutu wathunthu Amosi 6

Onani Amosi 6:2 nkhani